Macitidwe 17:13 BL92

13 Koma pamene Ayuda a ku Tesalonika anazindikira kuti mau a Mulungu analalikidwa ndi Paulo ku Bereyanso, anadza komwekonso, nautsa, nabvuta makamu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 17

Onani Macitidwe 17:13 nkhani