Macitidwe 19:16 BL92

16 Ndipo munthu, mwa iye amene munali mzimu woipa, anawalumphira nawaposa, nawalaka onse awiriwo, kotero kuti anathawa m'nyumba amarisece ndi olasidwa.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 19

Onani Macitidwe 19:16 nkhani