16 kuti, Tidzawacitira ciani anthu awa? pakutitu caoneka kwa onse akukhala m'Yerusalemu kuti cizindikilo cozindikirika cacitidwa ndi iwo, ndipo sitingathe kukana.
Werengani mutu wathunthu Macitidwe 4
Onani Macitidwe 4:16 nkhani