32 Ndipo unyinji wa iwo akukhulupira anali wa mtima umodzi ndi moyo umodzi; ndipo sananena mmodzi kuti kanthu ka cuma anali naco ndi kace ka iye yekha; koma anali nazo zonse zodyerana.
Werengani mutu wathunthu Macitidwe 4
Onani Macitidwe 4:32 nkhani