1 Mbiri 11:19 BL92

19 nati, Pali Mulungu wanga, kukhale kutali kwa ine kucita ici. Ngati ndidzamwa mwazi wa anthu awa? Akadataya moyo wao, inde akadataya moyo wao, pakukatenga madziwa. M'mwemo sanafuna kuwamwa. Izi anazicita atatu amphamvuwa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 11

Onani 1 Mbiri 11:19 nkhani