1 Mbiri 12:31 BL92

31 Ndipo a pfuko la Manase logawika pakati zikwi khumi mphambu zisanu ndi zitatu, ochulidwa maina ao kuti adzalonge Davide mfumu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 12

Onani 1 Mbiri 12:31 nkhani