1 Mbiri 21:23 BL92

23 Ndipo Orinani anati kwa Davide, Mulitenge, ndi mbuye wanga mfumu icite comkomera m'maso mwace; taonani, ndikupatsani ng'ombe za nsembe zopsereza; ndi zipangizo zopunthira zikhale nkhuni, ndi tirigu wa nsembe yaufa; ndizipereka zonse.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 21

Onani 1 Mbiri 21:23 nkhani