1 Mbiri 25:1 BL92

1 Ndipo Davide ndi akazembe a gulu la nkhondo anapatulira utumikiwo ena a ana a Asafu, ndi a Hemani, ndi a Yedutuni, anenere ndi azeze, ndi zisakasa, ndi nsanje; ndi ciwerengo ca anchito monga mwa kutumikira kwao ndko:

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 25

Onani 1 Mbiri 25:1 nkhani