1 Mbiri 25:6 BL92

6 Onsewa anawalangiza ndi atate wao ayimbe m'nyumba ya Yehova ndi nsanje, zisakasa ndi azeze; atumikire nazo m'nyumba ya Mulungu; ndipo Asafu, Yedutuni, ndi Hemani, anawalangiza ndi mfumu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 25

Onani 1 Mbiri 25:6 nkhani