19 nimupatse Solomo mwana wanga mtima wangwiro kusunga malamulo anu, mboni zanu, ndi malemba anu, ndi kucita izi zonse, ndi kumanga cinyumbaci cimene ndakonzeratu mirimo yace,
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 29
Onani 1 Mbiri 29:19 nkhani