1 Mbiri 29:20 BL92

20 Ndipo Davide anati kwa khamu lonse, Mulemekeze tsono Yehova Mulungu wanu. Ndi khamu lonse linalemekeza Yehova Mulungu wa makolo ao, nawerama, nalambira Yehova, ndi mfumu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 29

Onani 1 Mbiri 29:20 nkhani