1 Mbiri 6:63 BL92

63 Ana a Merari analandira mwa maere monga mwa mabanja ao, motapa pa pfuko la Rubeni, ndi pa pfuko la Gadi, ndi pa pfuko la Zebuluni, midzi khumi ndi iwiri.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 6

Onani 1 Mbiri 6:63 nkhani