7 Comweco Davide analetsa anyamata ace ndi mau awa, osawaloleza kuukira Sauli. Ndipo Sauli ananyamuka, naturuka m'phangamo, namuka njira yace.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 24
Onani 1 Samueli 24:7 nkhani