Macitidwe 18:5 BL92

5 Koma pamene Sila ndi Timoteo anadza potsika ku Makedoniya, Paulo anapsinjidwa ndi mau, nacitira umboni kwa Ayuda kuti Yesu ndiye Kristu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 18

Onani Macitidwe 18:5 nkhani