10 Ndipo pamene padauka cipolowe cacikuru, kapitao wamkuru anaopa kuti angamkadzule Paulo, ndipo analamulira asilikari atsike, namkwatule pakati pao, nadze naye kulowa naye m'linga,
Werengani mutu wathunthu Macitidwe 23
Onani Macitidwe 23:10 nkhani