Macitidwe 23:9 BL92

9 Ndipo cidauka cipolowe cacikuru; ndipo alembi ena a kwa Afarisi anaimirira, natsutsana, nanena, Sitipeza coipa ciri conse mwa munthuyu; ndipo nanga bwanji ngati mzimu kapena mngelo: walankhula naye?

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 23

Onani Macitidwe 23:9 nkhani