Macitidwe 25:10 BL92

10 Koma Paulo anati, ndirikuimirira pa mpando waciweruziro wa Kaisara, pompano ndiyenera kuweruzidwa ine; Ayuda sindinawacitira-kanthu koipa, monga mudziwanso nokha bwino.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 25

Onani Macitidwe 25:10 nkhani