26 ndi kuti,Pita kwa anthu awa, nuti,Ndi kumva mudzamva, ndipo simudzazindikira konse;Ndipo pakupenya mudzapenya, koma osaona konse;
27 Pakuti mtima wa anthu awa watupatu,Ndipo m'makutu mwao mmolemakumva,Ndipo masoao anawatseka;Kuti angaone ndi maso,Nangamve ndi makutu,Nangazindikire ndi mtima,Nangatembenuke,Ndipo Ine ndingawaciritse.
28 Potero, dziwani inu, kuti cipulumutso ici ca Mulungu citumidwa kwa amitundu; iwonsoadzamva. [
29 ]
30 Ndipo anakhala zaka ziwiri zamphumphu m'nyumba yace yobwereka, nalandira onse akufika kwa iye,
31 ndi kulalikira Ufumu wa Mulungu, ndi kuphunzitsa za Ambuye Yesu Kristu ndi kulimbika konse, wosamletsa munthu.