13 Mulungu wa Abrahamu, ndi Isake, ndi Yakobo, Mulungu wa makolo athu, analemekeza Mwana wace Yesu; amene, inu munampereka ndi kumkaniza pa Pilato, poweruza iyeyu kummasula.
Werengani mutu wathunthu Macitidwe 3
Onani Macitidwe 3:13 nkhani