Macitidwe 6:2 BL92

2 Ndipo khumi ndi awiriwo anaitana unyinji wa ophunzira, nati, Sikuyenera kuti ife tisiye mau a Mulungu ndi kutumikira podyerapo.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 6

Onani Macitidwe 6:2 nkhani