Macitidwe 7:10 BL92

10 namlanditsa iye m'zisautso zace zonse, nampatsa cisomo ndi nzeru pamaso pa Farao mfumu ya ku Aigupto; ndipo anamuika iye kazembe wa pa Aigupto ndi pa nyumba yace yonse.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 7

Onani Macitidwe 7:10 nkhani