11 Ndipo Ambuye anati kwa iye, Tauka, pita ku khwalala lochedwa Lolunjika, ndipo m'nyumba ya Yuda ufunse za munthu dzina lace Saulo, wa ku Tariso: pakuti taona, alikupemphera
Werengani mutu wathunthu Macitidwe 9
Onani Macitidwe 9:11 nkhani