2 Mbiri 13:18 BL92

18 Momwemo anacepetsedwa ana a Israyeli nthawi ija, nalakika ana a Yuda; popeza anatama Yehova Mulungu wa makolo ao.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 13

Onani 2 Mbiri 13:18 nkhani