1 Momwemo Abiya anagona ndi makolo ace, ndipo anamuika m'mudzi wa Davide; ndi Asa mwana wace anakhala mfumu m'malo mwace, m'masiku ace dziko linaona bata zaka khumi.
Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 14
Onani 2 Mbiri 14:1 nkhani