14 Ndipo anakantha midzi yonse pozungulira pace pa Gerari; a pakuti mantha ocokera kwa Yehova anawagwera; ndipo anafunkha m'midzi monse, pakuti mudacuruka zofunkha m'menemo.
Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 14
Onani 2 Mbiri 14:14 nkhani