2 Mbiri 24:12 BL92

12 Ndipo mfumu ndi Yehoyada anazipereka kwa iwo akugwira nchito ya utumiki ya nyumba ya Yehova, nalembera amisiri omanga ndi miyala, ndi osema mitengo, akonzenso nyumba ya Yehova; ndiponso akucita ndi citsulo ndi mkuwa alimbitse nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 24

Onani 2 Mbiri 24:12 nkhani