2 Mbiri 25:4 BL92

4 Koma sanapha ana ao, koma anacita monga umo mulembedwa m'cilamulo, m'buku la Mose, monga Yehova analamulira, ndi kuti, Atate asafere ana, ndi ana asafere atate; koma yense afere chimo lace lace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 25

Onani 2 Mbiri 25:4 nkhani