2 Mbiri 28:13 BL92

13 nanena nao, Musalowa nao andende kuno; pakuti inu mukuti mutiparamulitse kwa Yehova, kuonjezera pa macimo athu ndi zoparamula zathu; pakuti taparamula kwakukuru, ndipo pali mkwiyo waukali pa Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 28

Onani 2 Mbiri 28:13 nkhani