2 Mbiri 31:19 BL92

19 panalinso amuna mwa ana a Aroni ansembe, okhala m'minda ya kubusa kwa midzi yao, m'mudzi uli wonse, ochulidwa maina ao, agawire amuna onse mwa ansembe, ndi onse mwa Alevi, oyesedwa mwa cibadwidwe magawo ao.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 31

Onani 2 Mbiri 31:19 nkhani