2 Mbiri 32:8 BL92

8 pamodzi ndi iye pali dzanja la thupi lanyama; koma pamodzi ndi ife pali Yehova Mulungu wathu, kutithandiza ndi kutigwirira nkhondo. Ndipo anthu anacirikizika ndi mau a Hezekiya mfumu ya Yuda.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 32

Onani 2 Mbiri 32:8 nkhani