2 Mbiri 33:9 BL92

9 Koma Manase analakwitsa Yuda ndi okhala m'Yerusalemu, kotero kuti anacita coipa koposa amitundu, amene Yehova anawaononga pamaso pa ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 33

Onani 2 Mbiri 33:9 nkhani