2 Mbiri 35:20 BL92

20 Citatha ici conse, Yosiya atakonza nyumbayi, Neko mfumu ya Aigupto anakwera kuyambana ku Karikemisi ku Firate; ndipo Yosiya anamturukira kuyambana naye.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 35

Onani 2 Mbiri 35:20 nkhani