13 Kulemera kwace tsono kwa golidi anafika kwa Solomo caka cimodzi ndiko matalente mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi limodzi a golidi;
Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 9
Onani 2 Mbiri 9:13 nkhani