2 Mbiri 9:29 BL92

29 Macitidwe ena tsono a Solomo, oyamba ndi otsiriza, salembedwa kodi m'buku la mau a Natani mneneri ndi m'zonenera za Ahiya wa ku Silo, ndi m'masomphenya a Ido mlauli za Yerobiamu mwana wa Nebati?

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 9

Onani 2 Mbiri 9:29 nkhani