4 Atero Yehova, Musamuka kukayambana ndi abale anu, bwererani yense ku nyumba yace; pakuti cinthu ici cifuma kwa Ine. Ndipo anamvera mau a Yehova, nabwerera osakayambana ndi Yerobiamu.
Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 11
Onani 2 Mbiri 11:4 nkhani