2 Mbiri 24:27 BL92

27 Za ana ace tsono, ndi katundu wamkuru anamsenza, ndi kumanganso kwa nyumba ya Mulungu, taonani, zilembedwa m'buku lomasulira la mafumu. Ndipo Amaziya mwana wace anakhala mfumu m'malo mwace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 24

Onani 2 Mbiri 24:27 nkhani