15 Pamenepo mkwiyo wa Mulungu unayakira Amaziya, ndipo anamtumira mneneri amene anati, Mwafuniranji milungu ya anthu imene siinalanditsa anthu ao m'dzanja lanu?
Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 25
Onani 2 Mbiri 25:15 nkhani