2 Mbiri 25:27 BL92

27 Ndipo cipambukire Amaziya kusatsata Yehova, anamcitira ciwembu m'Yerusalemu, nathawira ku Lakisi iyeyu; koma anatuma omtsatira ku Lakisi, namupha komweko.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 25

Onani 2 Mbiri 25:27 nkhani