2 Mbiri 27:2 BL92

2 Ndipo anacita zoongoka pamaso pa Yehova, monga umo adacitira atate wace Uziya; pokhapo sanalowa m'Kacisi wa Yehova. Koma anthu anacitabe zobvunda.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 27

Onani 2 Mbiri 27:2 nkhani