2 Mbiri 33:13 BL92

13 Anampempha, ndipo anapembedzeka, namvera kupembedza kwace, nambwezera ku Yerusalemu m'ufumu wace. Pamenepo anadziwa Manase kuti Yehova ndiye Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 33

Onani 2 Mbiri 33:13 nkhani