2 Mbiri 33:14 BL92

14 Citatha ici tsono iye anaumangira mudzi wa Davide linga lakunja, kumadzulo kwa Gihoni, m'cigwa, mpaka polowera pa cipata cansomba; nazinga Ofeli, nalikweza kwambiri; anaikanso akazembe a nkhondo m'midzi yonse yamalinga ya m'Yuda.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 33

Onani 2 Mbiri 33:14 nkhani