5 Yehoyakimu anali wa zaka makumi awiri mphambu zisanu polowa ufumu wace, nakhala mfumu m'Yerusalemu zaka khumi ndi cimodzi, nacita coipa pamaso pa Yehova Mulungu wace.
Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 36
Onani 2 Mbiri 36:5 nkhani