2 Mbiri 8:11 BL92

11 Ndipo Solomo anamkweretsa mwana wamkazi wa Farao m'mudzi wa Davide, alowe m'nyumba imene adammangira; pakuti anati, Mkazi wanga asakhale m'nyumba ya Davide mfumu ya Israyeli; popeza mpopatulika pamene panafika likasa la Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 8

Onani 2 Mbiri 8:11 nkhani