2 Anakhala mfumu m'Yerusalemu zaka zitatu; ndi dzina la mace ndiye Mikaya mwana wamkazi wa Uriyeli wa ku Gibeya. Ndipo panali nkhondo pakati pa Abiya ndi Yerobiamu.
Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 13
Onani 2 Mbiri 13:2 nkhani