2 Mbiri 25:9 BL92

9 Ndipo Amaziya anati kwa munthu wa Mulungu, Koma nanga titani nao matalente zana limodzi ndinapatsa ankhondo a Israyeli? Nati munthu wa Mulungu, Yehova ali nazo zoposa izi kukupatsani.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 25

Onani 2 Mbiri 25:9 nkhani