2 Mbiri 33:19 BL92

19 Pemphero lace lomwe, ndi m'mene Mulungu anapembedzeka naye, ndi chimo lace lonse, ndi kulakwa kwace, ndi apo anamanga misanje, naimika zifanizo ndi mafano osema asanadzicepetse, taonani, zalembedwa m'buku la mau a Hozai.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 33

Onani 2 Mbiri 33:19 nkhani