Eksodo 12:4 BL92

4 Banja likaperewera mwana wa nkhosa, munthu ndi mnzace ali pafupi pa nyumba yace atenge monga mwa kufikira kwa anthu ao; muziwerengera mwana wa nkhosa monga mwa kudya kwao.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 12

Onani Eksodo 12:4 nkhani