Eksodo 12:48 BL92

48 Koma akakhala nanu mlendo, nakonzera Yehova Paskha, adulidwe amuna ace onse, ndipo pamenepo asendere kuucita; nakhale ngati wobadwa m'dziko; koma wosadulidwa ali yense asadyeko.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 12

Onani Eksodo 12:48 nkhani