Eksodo 18:25 BL92

25 Ndipo Mose anasankha amuna amtima mwa Aisrayeli onse, nawaika akuru a pa anthu, akuru a pa zikwi, akuru a pa mazana, akuru a pa makumi asanu, ndi akuru a pa makumi.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 18

Onani Eksodo 18:25 nkhani