Eksodo 18:8 BL92

8 Ndipo Mose anafotokozera mpongozi wace zonse Yehova adazicitira Farao ndi Aaigupto cifukwa ca Israyeli; ndi mabvuto onse anakomana nao panjira, ndi kuti Yehova adawalanditsa.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 18

Onani Eksodo 18:8 nkhani